Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 20:2 - Buku Lopatulika

2 Natumiza mithenga kumzinda kwa Ahabu mfumu ya Israele, nati kwa iye,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Natumiza mithenga kumudzi kwa Ahabu mfumu ya Israele, nati kwa iye,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Tsono Benihadadi adatuma amithenga ake kwa Ahabu mumzindamo kukamuuza mau akuti

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Iye anatuma amithenga ake mu mzindamo kwa Ahabu mfumu ya Israeli, kukanena kuti,

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 20:2
6 Mawu Ofanana  

Tsono Asa anatenga siliva yense ndi golide yense anatsala pa chuma cha nyumba ya Yehova, ndi chuma chili m'nyumba ya Yehova chuma chili m'nyumba ya mfumu, nazipereka m'manja mwa anyamata ake; ndipo mfumu Asa anazitumiza kwa Benihadadi mwana wa Tabirimoni, mwana wa Heziyoni mfumu ya Aramu, wakukhala ku Damasiko, nati,


Ndipo Benihadadi mfumu ya Aramu anamemeza khamu lake lonse la nkhondo; ndi mafumu makumi atatu mphambu awiri anali naye, pamodzi ndi akavalo ndi magaleta; nakamangira Samariya misasa, naponyana nao nkhondo.


Atero Benihadadi, Siliva wako ndi golide wako ndi wanga, akazi ako ndi ana ako omwe okometsetsawo ndi anga.


Ndipo anamva za Tirihaka mfumu ya Kusi, akuti, Taonani, watuluka kuthirana nawe nkhondo. Pamenepo anatumizanso mithenga kwa Hezekiya, ndi kuti,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa