1 Mafumu 2:6 - Buku Lopatulika6 Chita mwa nzeru yako tsono, osalola mutu wake waimvi utsikire kumanda ndi mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Chita mwa nzeru yako tsono, osalola mutu wake waimvi utsikire kumanda ndi mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono iwe uchite potsata nzeru zako, koma ndithu usalole kuti afe ndi ukalamba ndi kupita ku manda mwamtendere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iwe uchite kwa iye molingana ndi nzeru zako, koma usalole kuti afe ndi ukalamba ndi kupita ku manda mwamtendere. Onani mutuwo |