1 Mafumu 2:4 - Buku Lopatulika4 kuti Yehova akakhazikitse mau ake adanenawo za ine, kuti, Ngati ana ako akasunga bwino njira zao, kuyenda moona pamaso pa Ine ndi mtima wao wonse ndi moyo wao wonse, nditi sipadzakusowa mwamuna mmodzi pa mpando wachifumu wa Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 kuti Yehova akakhazikitse mau ake adanenawo za ine, kuti, Ngati ana ako akasunga bwino njira zao, kuyenda moona pamaso pa Ine ndi mtima wao wonse ndi moyo wao wonse, nditi sipadzakusowa mwamuna mmodzi pa mpando wachifumu wa Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Uzitero kuti Chauta achitedi zimene adalankhula za ine kuti, ‘Ana ako aamuna akamasamala makhalidwe ao ndi kukhala okhulupirika kwa Ine ndi mtima wao wonse ndi mzimu wao wonse, sipadzasoŵa munthu pa banja lako wolamulira Israele.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndipo Yehova akwaniritse zimene anandilonjeza kuti, ‘Ngati zidzukulu zako zidzakhala mosamala, niziyenda mokhulupirika pamaso panga ndi mtima wawo wonse ndi moyo wawo wonse, sudzasowa munthu wokhala pa mpando waufumu wa Israeli.’ Onani mutuwo |