1 Mafumu 2:2 - Buku Lopatulika2 Ndimuka ine njira ya dziko lonse: limba mtima tsono, nudzionetse umunthu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndimuka ine njira ya dziko lonse: limba mtima tsono, nudzionetse umunthu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Ine ndi ulendo uno, nchifukwa chake tsono khala wamphamvu ndipo ulimbike mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Ndatsala pangʼono kupita kumene munthu wina aliyense amayenera kupitako. Tsono khala wamphamvu, uvale zilimbe, Onani mutuwo |