Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 2:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo Bateseba anati, Chabwino, ndidzakunenera kwa mfumu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo Bateseba anati, Chabwino, ndidzakunenera kwa mfumu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Bateseba adati, “Chabwino. Ndikulankhulira kwa mfumu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Batiseba anayankha kuti, “Chabwino. Ndidzakuyankhulira kwa mfumu.”

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 2:18
3 Mawu Ofanana  

Nati iye, Mundinenere kwa mfumu Solomoni, popeza sakukanizani, kuti andipatse Abisagi wa ku Sunamu akhale mkazi wanga.


Tsono Bateseba ananka kwa mfumu Solomoni kukanenera Adoniya kwa iye. Ndipo mfumu inanyamuka kukomana naye, namuweramira nakhalanso pa mpando wake wachifumu, naikitsa mpando wina wa amake wa mfumu, nakhala iye ku dzanja lake lamanja.


Wachibwana akhulupirira mau onse; koma wochenjera asamalira mayendedwe ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa