1 Mafumu 2:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo tsopano, ndikupemphani pempho limodzi, musandikaniza. Ndipo mkaziyo anati kwa iye, Tanena. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo tsopano, ndikupemphani pempho limodzi, musandikaniza. Ndipo mkaziyo anati kwa iye, Tanena. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tsopano ndikukupemphani chinthu chimodzi. Musandikanize ai.” Bateseba adati, “Nena.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Tsono ndili ndi pempho limodzi kwa inu. Musandikanize ayi.” Batiseba anati, “Nena.” Onani mutuwo |