1 Mafumu 2:12 - Buku Lopatulika12 Tsono Solomoni anakhala pa mpando wachifumu wa Davide atate wake, ndipo ufumu wake unakhazikika kwakukulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Tsono Solomoni anakhala pa mpando wachifumu wa Davide atate wake, ndipo ufumu wake unakhazikika kwakukulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Choncho Solomoni adakhala pa mpando waufumu wa Davide atate ake. Ndipo ufumu wake unali wokhazikika kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Choncho Solomoni anakhala pa mpando waufumu wa abambo ake Davide, ndipo ufumu wake unakhazikika kwambiri. Onani mutuwo |