1 Mafumu 2:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo Davide anagona pamodzi ndi makolo ake, naikidwa m'mzinda wa Davide. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo Davide anagona pamodzi ndi makolo ake, naikidwa m'mudzi wa Davide. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tsono Davide adamwalira, naikidwa m'manda mu mzinda wake wa Davideyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Tsono Davide anamwalira ndipo anayikidwa mʼmanda mu Mzinda wa Davide. Onani mutuwo |