1 Mafumu 2:1 - Buku Lopatulika1 Pakuyandikira masiku ake a Davide akuti amwalire, analamulira Solomoni mwana wake, nati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pakuyandikira masiku ake a Davide akuti amwalire, analamulira Solomoni mwana wake, nati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nthaŵi yoti Davide amwalire itayandikira, adauza mwana wake Solomoni kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Davide ali pafupi kumwalira, analangiza mwana wake Solomoni kuti: Onani mutuwo |