1 Mafumu 18:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Ahabu anaitana Obadiya woyang'anira nyumba yake. Koma Obadiya anaopa ndithu Yehova; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Ahabu anaitana Obadiya woyang'anira nyumba yake. Koma Obadiya anaopa ndithu Yehova; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mfumu Ahabu adaitana Obadiya, amene ankayang'anira zonse za ku nyumba yachifumu. (Ndiye kuti Obadiya ankatumikira Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 ndipo Ahabu anayitana Obadiya amene ankayangʼanira nyumba yake yaufumu. (Obadiya ankaopa Yehova kwambiri. Onani mutuwo |