1 Mafumu 18:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Eliya ananka kukadzionetsa kwa Ahabu. Ndipo njala inali yaikulu mu Samariya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Eliya ananka kukadzionetsa kwa Ahabu. Ndipo njala inali yaikulu m'Samariya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Motero Eliya adapita kukadziwonetsa kwa Ahabu. Pamenepo nkuti njala itafika pake penipeni ku Samariya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Choncho Eliya anapita kukadzionetsa kwa Ahabu. Tsono nthawi imeneyi njala inakula kwambiri mu Samariya, Onani mutuwo |