1 Mafumu 17:9 - Buku Lopatulika9 Nyamuka, pita ku Zarefati wa ku Sidoni, nukhale kumeneko; taona, ndamlamulira mkazi wamasiye wa kumeneko akudyetse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Nyamuka, pita ku Zarefati wa ku Sidoni, nukhale kumeneko; taona, ndamlamulira mkazi wamasiye wa kumeneko akudyetse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Nyamuka upite ku Zarefati, mudzi wa ku Sidoni, ndipo ukakhale kumeneko. Ndalamula mai wamasiye wakumeneko kuti azikakudyetsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Nyamuka tsopano, pita ku Zarefati ku Sidoni ndipo ukakhale kumeneko. Ndalamula mkazi wamasiye wa kumeneko kuti azikakudyetsa.” Onani mutuwo |