1 Mafumu 17:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo kudzakhala kuti uzikamwa mumtsinje, ndipo ndalamulira makwangwala kukudyetsa kumeneko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo kudzakhala kuti uzikamwa mumtsinje, ndipo ndalamulira makungubwi kukudyetsa kumeneko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Uzikamwa mumtsinjemo, ndipo ndalamula makwangwala kuti azikakudyetsa kumeneko.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Uzikamwa mu mtsinjemo, ndipo ndalamula makwangwala kuti azikakudyetsa kumeneko.” Onani mutuwo |