1 Mafumu 17:3 - Buku Lopatulika3 Choka kuno, nutembenukire kum'mawa, ukabisale kumtsinje Keriti uli ku Yordani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Choka kuno, nutembenukire kum'mawa, ukabisale kumtsinje Keriti uli ku Yordani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 “Chokako kuno, upite chakuvuma, ukabisale ku mtsinje wa Keriti, kuvuma kwa Yordani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 “Choka kuno, upite kummawa, ukabisale mʼmbali mwa mtsinje wa Keriti, pafupi ndi Yorodani. Onani mutuwo |