Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 17:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo mau a Yehova anadza kwa iye, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo mau a Yehova anadza kwa iye, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Kenaka Chauta adauza Eliyayo kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Pamenepo Yehova anayankhula ndi Eliya kuti,

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 17:2
9 Mawu Ofanana  

Ndipo mau a Mulungu anafika kwa Semaya mneneri wa Mulungu, nati,


Ndipo Eliya wa ku Tisibe wokhala ku Giliyadi ananena ndi Ahabu, nati, Pali Yehova Mulungu wa Israele, amene ndimakhala pamaso pake, ngati adzagwa mame kapena mvula zaka izi, koma ntanena ine ndipo.


Choka kuno, nutembenukire kum'mawa, ukabisale kumtsinje Keriti uli ku Yordani.


Ndipo mau a Yehova anadza kwa iye, nati,


Ndipo usiku womwewo mau a Mulungu anadzera Natani, ndi kuti,


Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,


Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,


Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa