Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 16:4 - Buku Lopatulika

4 Agalu adzadya aliyense wa Baasa amene adzafera m'mzinda, ndipo amene adzafera m'thengo zidzamudya mbalame za m'mlengalenga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Agalu adzadya aliyense wa Baasa amene adzafera m'mudzi, ndipo amene adzafera m'thengo zidzamudya mbalame za m'mlengalenga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Aliyense wa banja la Baasa amene adzafere mu mzinda, agalu adzamudya. Ndipo aliyense amene adzafere ku thengo, mbalame zamumlengalenga zidzamudya.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Agalu adzadya aliyense wa banja la Baasa amene adzafere mu mzinda, ndipo mbalame za mu mlengalenga zidzadya iwo amene adzafere kuthengo.”

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 16:4
4 Mawu Ofanana  

Agalu adzadya aliyense wa Yerobowamu wakufa m'mzinda; ndi mbalame za m'mlengalenga zidzadya yense wakufera kuthengo; popeza wanena ndi Yehova.


Ndipo panali nkhondo pakati pa Asa ndi Baasa mfumu ya Israele masiku ao onse.


Mwana aliyense wa Ahabu amene adzafera m'mzinda, agalu adzamudya; ndipo iye amene adzafera kuthengo, mbalame za m'mlengalenga zidzamudya.


ndidzapereka iwo m'dzanja la adani ao, ndi m'dzanja la iwo akufuna moyo wao; ndipo mitembo yao idzakhala chakudya cha mbalame za mlengalenga, ndi cha zilombo za padziko lapansi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa