Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 15:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo chaka cha makumi awiri cha Yerobowamu mfumu ya Israele, Asa anayamba kukhala mfumu ya Yuda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo chaka cha makumi awiri cha Yerobowamu mfumu ya Israele, Asa anayamba kukhala mfumu ya Yuda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Pa chaka cha 20 cha ufumu wa Yerobowamu mfumu ya ku Israele, Asa adaloŵa ufumu wa ku Yuda,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Mʼchaka cha makumi awiri cha Yeroboamu mfumu ya Israeli, Asa anakhala mfumu ya Yuda,

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 15:9
5 Mawu Ofanana  

Nakhala mfumu mu Yerusalemu zaka makumi anai mphambu chimodzi, ndipo dzina la amake linali Maaka mwana wa Abisalomu.


Nagona Abiya ndi makolo ake, namuika anthu m'mzinda wa Davide; Asa mwana wake nalowa ufumu m'malo mwake.


Ndi Yerobowamu sanaonenso mphamvu m'masiku a Abiya, namkantha Yehova, nafa iye.


Momwemo Abiya anagona ndi makolo ake, ndipo anamuika m'mzinda wa Davide; ndi Asa mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake; m'masiku ake dziko linaona bata zaka khumi.


Ndipo pakumva Asa mau awa, ndi chinenero cha Odedi mneneriyo, analimbika mtima, nachotsa zonyansazo m'dziko lonse la Yuda ndi Benjamini, ndi m'mizinda adailanda ku mapiri a Efuremu; nakonza guwa la nsembe la Yehova lokhala pakhomo pachipinda cholowera cha nyumba ya Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa