1 Mafumu 15:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo chaka cha makumi awiri cha Yerobowamu mfumu ya Israele, Asa anayamba kukhala mfumu ya Yuda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo chaka cha makumi awiri cha Yerobowamu mfumu ya Israele, Asa anayamba kukhala mfumu ya Yuda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Pa chaka cha 20 cha ufumu wa Yerobowamu mfumu ya ku Israele, Asa adaloŵa ufumu wa ku Yuda, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mʼchaka cha makumi awiri cha Yeroboamu mfumu ya Israeli, Asa anakhala mfumu ya Yuda, Onani mutuwo |