1 Mafumu 15:3 - Buku Lopatulika3 Nayenda iye m'zoipa zonse za atate wake, zimene iye adachita asanalowe ufumu Abiyayo; ndipo mtima wake sunali wangwiro ndi Yehova Mulungu wake monga mtima wa Davide kholo lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Nayenda iye m'zoipa zonse za atate wake, zimene iye adachita asanalowe ufumu Abiyayo; ndipo mtima wake sunali wangwiro ndi Yehova Mulungu wake monga mtima wa Davide kholo lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndipo Abiyayo adatsatira zoipa zonse zimene ankachita bambo wake. Sadatsate Chauta moona monga Davide kholo lake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Abiya anachita zoyipa zonse zimene abambo ake anazichita. Sanali wangwiro pamaso pa Yehova Mulungu wake, monga linachitira kholo lake Davide. Onani mutuwo |