1 Mafumu 15:2 - Buku Lopatulika2 Anakhala mfumu zaka zitatu mu Yerusalemu, ndipo dzina la amake linali Maaka mwana wa Abisalomu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Anakhala mfumu zaka zitatu m'Yerusalemu, ndipo dzina la amake linali Maaka mwana wa Abisalomu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adakhala mfumu mu Yerusalemu zaka zitatu. Mai wake anali Maaka, mwana wa Abisalomu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 ndipo analamulira mu Yerusalemu zaka zitatu. Amayi ake anali Maaka, mwana wa Abisalomu. Onani mutuwo |