1 Mafumu 13:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo iye anapatsa chizindikiro tsiku lomwelo, nati, Chizindikiro chimene Yehova ananena ndi ichi, Taonani guwali la nsembe lidzang'ambika, ndi phulusa lili pa ilo lidzatayika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo iye anapatsa chizindikiro tsiku lomwelo, nati, Chizindikiro chimene Yehova ananena ndi ichi, Taonani guwali la nsembe lidzang'ambika, ndi phulusa lili pa ilo lidzatayika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono mneneri uja adapereka chizindikiro pa tsiku lomwelo nati, “Chizindikiro chimene Chauta wanena ndi ichi, ‘Guwali lidzang'ambika ndipo phulusa limene lili pamenepo lidzamwazika.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tsiku lomwelo munthu wa Mulungu uja anapereka chizindikiro ichi: “Chizindikiro chimene Yehova wanena ndi ichi: Taonani guwali lidzangʼambika pakati ndipo phulusa lili pamenepo lidzamwazika.” Onani mutuwo |