Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 13:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo onani, anthu anapitapo naona mtembo wogwera m'njiramo, ndi mkango uli chiimire pafupi ndi mtembo, nadzanena m'mzinda m'mene munakhala mneneri wokalamba uja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo onani, anthu anapitapo naona mtembo wogwera m'njiramo, ndi mkango uli chiimire pafupi ndi mtembo, nadzanena m'mudzi m'mene munakhala mneneri wokalamba uja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Anthu ena amene ankapita mumseumo, adaona mtembo uli gone, mkango utaima pambali pake. Ndipo adapita namakasimbira anzao mu mzinda za zimene adaaona pamseu paja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Ndipo taonani, anthu ena amene ankapita mu msewumo anaona mtembowo uli pansi potero, mkango utayima pa mbali pa mtembo uja ndipo anapita nakafotokozera anthu mu mzinda umene mumakhala mneneri wokalamba uja.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 13:25
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ku Betele kunakhala mneneri wokalamba, ndipo mwana wake wina anadzamfotokozera machitidwe onse anawachita munthu wa Mulunguyo tsiku lomwelo mu Betele ndi mau ake anawanena ndi mfumu; inde omwe aja iwo anamfotokozera atate wao.


Ndipo mneneri amene uja anambweza panjirayo atamva, anati, Ndiye munthu uja wa Mulungu amene sanamvere mau a Yehova; chifukwa chake Yehova wampereka kwa mkango, numkadzula numupha, monga mwa mau a Yehova analankhula nayewo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa