Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 13:13 - Buku Lopatulika

13 Nanena ndi ana ake, Ndimangireni mbereko pabulu. Namangira iwo mbereko pabulu, naberekekapo iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Nanena ndi ana ake, Ndimangireni mbereko pa bulu. Namangira iwo mbereko pa bulu, naberekekapo iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Bambo uja adauza ana akewo kuti, “Mangireni chishalo pa bulu.” Anawo adamanga chishalocho pa bulu, ndipo nkhalamba ija idakwerapo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Ndipo abambo aja anati kwa ana akewo, “Mangireni chishalo pa bulu.” Anawo atamangirira chishalo pa bulu, nkhalambayo inakwera buluyo

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 13:13
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anayankha, Mbuye wanga mfumu, mnyamata wanga anandinyenga; pakuti mnyamata wanu ndinati, Ndidzadzimangira bulu kuti ndiberekekepo ndi kupita ndi mfumu, pakuti mnyamata wanu ndili wopunduka.


Ndipo atate wao anati kwa iwo, Wapitira njira yiti? Popeza ana ake adaona njira analowera munthu wa Mulungu anachokera ku Yudayo.


Natsata munthu wa Mulungu, nampeza ali tsonga patsinde pa mtengo wathundu, nanena naye, Kodi ndiwe munthu wa Mulungu amene uja anachokera ku Yuda? Nati, Ndine amene.


Iye nanena ndi ana ake, nati, Ndimangireni mbereko pabulu. Namangira mbereko.


Pamenepo Balamu anauka m'mawa namanga bulu wake, namuka nao akalonga a ku Mowabu.


Ndipo anali nao ana aamuna makumi atatu okwera pa ana a abulu makumi atatu, iwo ndipo anali nayo mizinda makumi atatu, otchedwa midzi ya Yairi, mpaka lero lino, ndiyo m'dziko la Giliyadi.


Inu akuyenda okwera pa abulu oyera, inu akukhala poweruzira, ndi inu akuyenda m'njira, fotokozerani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa