Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 13:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo atate wao anati kwa iwo, Wapitira njira yiti? Popeza ana ake adaona njira analowera munthu wa Mulungu anachokera ku Yudayo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo atate wao anati kwa iwo, Wapitira njira yiti? Popeza ana ake adaona njira analowera munthu wa Mulungu anachokera ku Yudayo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Ndipo bambo wao uja adaŵafunsa kuti, “Kodi adadzera njira iti?” Ana akewo adamlangiza njira imene adadzera mneneri wa Mulungu wochokera ku Yuda uja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Abambo awo aja anawafunsa kuti, “Kodi wadzera njira iti?” Ana akewo anamufotokozera njira imene munthu wa Mulungu wochokera ku Yudayo anadzera.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 13:12
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ku Betele kunakhala mneneri wokalamba, ndipo mwana wake wina anadzamfotokozera machitidwe onse anawachita munthu wa Mulunguyo tsiku lomwelo mu Betele ndi mau ake anawanena ndi mfumu; inde omwe aja iwo anamfotokozera atate wao.


Nanena ndi ana ake, Ndimangireni mbereko pabulu. Namangira iwo mbereko pabulu, naberekekapo iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa