1 Mafumu 13:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo ku Betele kunakhala mneneri wokalamba, ndipo mwana wake wina anadzamfotokozera machitidwe onse anawachita munthu wa Mulunguyo tsiku lomwelo mu Betele ndi mau ake anawanena ndi mfumu; inde omwe aja iwo anamfotokozera atate wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo ku Betele kunakhala mneneri wokalamba, ndipo mwana wake wina anadzamfotokozera machitidwe onse anawachita munthu wa Mulunguyo tsiku lomwelo m'Betele ndi mau ake anawanena ndi mfumu; inde omwe aja iwo anamfotokozera atate wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono ku Betele kunkakhala mneneri wina wokalamba. Ana ake adadza kudzamuuza zonse zimene mneneri wa Mulungu adaachita ku Betele tsiku lija. Adauzanso atate ao mau onse amene mneneri wa Mulungu uja adaauza mfumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Tsono ku Beteli kunkakhala mneneri wina wokalamba. Mmodzi mwa ana ake anamufotokozera zonse zomwe munthu wa Mulungu anachita kumeneko tsiku limenelo. Anawuzanso abambo ake zimene ananena kwa mfumu. Onani mutuwo |