Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 13:10 - Buku Lopatulika

10 Tsono iye anayenda njira ina osabwerera njira yomweyo anaidzera pakudza ku Betele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Tsono iye anayenda njira ina osabwerera njira yomweyo anaidzera pakudza ku Betele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Motero mneneriyo adadzera njira ina, osatsata njira imene adaadzera popita ku Betele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Choncho munthu wa Mulunguyo anadzera njira ina ndipo sanatsate njira imene anayendamo pobwera ku Beteliko.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 13:10
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ku Betele kunakhala mneneri wokalamba, ndipo mwana wake wina anadzamfotokozera machitidwe onse anawachita munthu wa Mulunguyo tsiku lomwelo mu Betele ndi mau ake anawanena ndi mfumu; inde omwe aja iwo anamfotokozera atate wao.


Pakuti potero ndinalamulidwa ndi mau a Yehova, ndi kuti, Usakadye mkate, kapena kumwa madzi, kapena kubwerera njira yomweyo unadzerayo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa