1 Mafumu 13:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo onani, munthu wa Mulungu anachokera ku Yuda mwa mau a Yehova nadza ku Betele; ndipo Yerobowamu anali kuimirira m'mbali mwa guwa la nsembe kufukiza zonunkhira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo onani, munthu wa Mulungu anachokera ku Yuda mwa mau a Yehova nadza ku Betele; ndipo Yerobowamu anali kuimirira m'mbali mwa guwa la nsembe kufukiza zonunkhira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsono mneneri wa Mulungu adachokera ku Yuda napita ku Betele monga momwe Chauta adaamlamulira. Nthaŵi imeneyo nkuti Yerobowamu ataimirira pambali pa guwa akufukiza lubani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndipo taonani, munthu wa Mulungu wochokera ku Yuda anapita ku Beteli molamulidwa ndi Yehova. Nthawi imeneyo nʼkuti Yeroboamu atayimirira pambali pa guwa akufukiza lubani. Onani mutuwo |