1 Mafumu 12:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo anatuma kukamuitana. Ndipo Yerobowamu ndi msonkhano wonse wa Israele anadza, nalankhulana ndi Rehobowamu, nati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo anatuma kukamuitana. Ndipo Yerobowamu ndi msonkhano wonse wa Israele anadza, nalankhulana ndi Rehobowamu, nati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Anthu adakamuitana. Choncho Yerobowamu pamodzi ndi anthu onse a ku Israele adadza kwa Rehobowamu namuuza kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tsono anthu anayitanitsa Yeroboamu, ndipo iye pamodzi ndi gulu lonse la ku Israeli anapita kwa Rehobowamu ndipo anamuwuza kuti, Onani mutuwo |