1 Mafumu 11:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Yehova anakwiya ndi Solomoni, pokhala mtima wake unapatuka kwa Yehova Mulungu wa Israele, amene adamuonekera kawiri, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Yehova anakwiya ndi Solomoni, pokhala mtima wake unapatuka kwa Yehova Mulungu wa Israele, amene adamuonekera kawiri, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Choncho Chauta adakwiyira Solomoni, chifukwa choti mtima wake udaasinthika ndi kusiya Chauta, Mulungu wa Aisraele, amene adamuwonekera kaŵiri konse, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Choncho Yehova anakwiyira Solomoni chifukwa mtima wake unatembenuka kuchoka kwa Yehova Mulungu wa Israeli, amene anamuonekera kawiri konse. Onani mutuwo |