Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 11:41 - Buku Lopatulika

41 Ndipo machitidwe otsiriza a Solomoni, ndi ntchito zake zonse anazichita, ndi nzeru zake, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a Solomoni?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

41 Ndipo machitidwe otsiriza a Solomoni, ndi ntchito zake zonse anazichita, ndi nzeru zake, sizinalembedwa kodi m'buku la machitidwe a Solomoni?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

41 Tsono ntchito zina za Solomoni, ndi zonse zimene adachita, ndiponso nzeru zake, zidalembedwa m'buku la Ntchito za Solomoni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

41 Ntchito zina za Solomoni, zonse zomwe anachita komanso za nzeru zake, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya Solomoni?

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 11:41
2 Mawu Ofanana  

Ndipo masiku amene Solomoni anakhala mfumu ya Aisraele onse mu Yerusalemu anali zaka makumi anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa