1 Mafumu 10:8 - Buku Lopatulika8 Odala anthu anu, odala anyamata anu akukhala nthawi zonse pamaso panu, akumvaimva nzeru yanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Odala anthu anu, odala anyamata anu akukhala nthawi zonse pamaso panu, akumvaimva nzeru yanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ngodala anthu anu. Ngodala atumiki anuŵa, amene amaima pamaso panu nthaŵi zonse ndi kumamva nzeru zanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ngodala anthu anu! Ngodala atumiki anu amene amayimirira pamaso panu nthawi zonse ndi kumamva nzeru zanu! Onani mutuwo |