1 Mafumu 10:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo mfumu Solomoni ananinkha mfumu yaikazi ya ku Sheba chifuniro chake chonse anachipempha iye, osawerenga chimene Solomoni anamninkha mwa ufulu wake. Momwemo iye anabwerera namukanso ku dziko lake, iyeyo ndi anyamata ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo mfumu Solomoni ananinkha mfumu yaikazi ya ku Sheba chifuniro chake chonse anachipempha iye, osawerenga chimene Solomoni anamninkha mwa ufulu wake. Momwemo iye anabwerera namukanso ku dziko lake, iyeyo ndi anyamata ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mfumu Solomoni adapatsa mfumukazi ya ku Sheba ija zonse zimene inkafuna, ndiponso chilichonse chimene idaapempha, osaŵerengera mphatso zachifumu zimene anali ataipatsa kale. Tsono mfumukaziyo idabwerera ku dziko lakwao pamodzi ndi atumiki ake aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Mfumu Solomoni inapereka kwa mfumu yayikazi ya ku Seba zonse zimene inazifuna ndi kuzipempha, osawerengera mphatso zaufumu zimene anali atamupatsa. Choncho inabwerera ku dziko la kwawo pamodzi ndi atumiki ake. Onani mutuwo |