1 Mafumu 1:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anapangana ndi Yowabu mwana wa Zeruya, ndi Abiyatara wansembeyo; ndipo amenewo anamtsata Adoniya namthandiza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anapangana ndi Yowabu mwana wa Zeruya, ndi Abiyatara wansembeyo; ndipo amenewo anamtsata Adoniya namthandiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Iyeyo adapangana ndi Yowabu, mwana wa Zeruya, ndiponso Abiyatara wansembe. Choncho iwowo adamtsata Adoniya namamthandiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Adoniya anagwirizana ndi Yowabu mwana wa Zeruya ndiponso Abiatara wansembe, ndipo iwowa anamuthandiza. Onani mutuwo |