Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 1:43 - Buku Lopatulika

43 Ndipo Yonatani anayankha, nati kwa Adoniya, Zedi Davide mbuye wathu mfumu walonga Solomoni ufumu:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

43 Ndipo Yonatani anayankha, nati kwa Adoniya, Zedi Davide mbuye wathu mfumu walonga Solomoni ufumu:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

43 Tsono Yonatani adayankha kuti, “Iyai, zinthu zaipa uku! Mbuyathu mfumu Davide walonga Solomoni ufumu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

43 Yonatani anayankha Adoniya kuti, “Ayi ndithu, zinthu sizili bwino! Mbuye wathu Mfumu Davide walonga Solomoni ufumu.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 1:43
2 Mawu Ofanana  

Iye akali chilankhulire, taona, walowa Yonatani mwana wa Abiyatara wansembe, ndipo Adoniya anati, Lowa, popeza ndiwe munthu wamphamvu, nubwera nao uthenga wabwino.


ndipo mfumu yatumanso Zadoki wansembe, ndi Natani mneneri, ndi Benaya mwana wa Yehoyada, ndi Akereti, ndi Apeleti aja, namkweza iye pa nyuru ya mfumu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa