1 Mafumu 1:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo Bateseba anawerama nalambira mfumu, ndi mfumu niti, Ufunanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo Bateseba anawerama nalambira mfumu, ndi mfumu niti, Ufunanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Bateseba adagwada nalambira mfumu. Tsono mfumu idamufunsa kuti, “Kodi nkwabwino?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Batiseba anagwada nalambira mfumu. Mfumu inamufunsa kuti, “Kodi nʼchiyani chimene ukufuna?” Onani mutuwo |