1 Mafumu 1:12 - Buku Lopatulika12 Ubwere tsono, ndikupangire, kuti usunge moyo wako, ndi moyo wa mwana wako Solomoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ubwere tsono, ndikupangire, kuti usunge moyo wako, ndi moyo wa mwana wako Solomoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Nchifukwa chake tsono ndikupatseni nzeru kuti mupulumutse moyo wanu pamodzi ndi moyo wa mwana wanu Solomoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Tsopano ine ndikulangizeni inu mmene mungapulumutsire moyo wanu ndi moyo wa mwana wanu Solomoni. Onani mutuwo |