1 Mafumu 1:10 - Buku Lopatulika10 koma Natani mneneriyo, ndi Benaya, ndi anthu amphamvu aja, ndi Solomoni mbale wake, sanawaitane. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 koma Natani mneneriyo, ndi Benaya, ndi anthu amphamvu aja, ndi Solomoni mbale wake, sanawaitane. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Koma sadaitaneko mneneri Natani, Benaya, anthu amphamvu aja a mfumu Davide, kapenanso Solomoni mbale wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 koma sanayitane mneneri Natani kapena Benaya kapenanso asilikali amphamvu a Davide ngakhalenso mʼbale wake Solomoni. Onani mutuwo |