1 Akorinto 9:26 - Buku Lopatulika26 Chifukwa chake ine ndithamanga chotero, si monga chosinkhasinkha. Ndilimbana chotero, si monga ngati kupanda mlengalenga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Chifukwa chake ine ndithamanga chotero, si monga chosinkhasinkha. Ndilimbana chotero, si monga ngati kupanda mlengalenga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Nchifukwa chake ndimathamanga monga munthu wodziŵa kumene walinga. Ndiponso ndikamachita mpikisano womenyana, sindichita ngati munthu amene angomenya mophonya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Choncho sindithamanga monga wothamanga wopanda cholinga; komanso sindichita mpikisano wankhonya monga munthu amene amangomenya mophonya. Onani mutuwo |