1 Akorinto 7:33 - Buku Lopatulika33 koma iye wokwatira alabadira zinthu za dziko lapansi, kuti akondweretse mkazi wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 koma iye wokwatira alabadira zinthu za dziko lapansi, kuti akondweretse mkazi wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Koma munthu wokwatira amatekeseka ndi zapansipano, kuganiza za m'mene angakondweretsere mkazi wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Koma wa pa banja amalabadira za dziko lapansi lino, mmene angakondweretsere mkazi wake, Onani mutuwo |