Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 7:33 - Buku Lopatulika

33 koma iye wokwatira alabadira zinthu za dziko lapansi, kuti akondweretse mkazi wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 koma iye wokwatira alabadira zinthu za dziko lapansi, kuti akondweretse mkazi wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Koma munthu wokwatira amatekeseka ndi zapansipano, kuganiza za m'mene angakondweretsere mkazi wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Koma wa pa banja amalabadira za dziko lapansi lino, mmene angakondweretsere mkazi wake,

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 7:33
13 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anati kwa ophunzira ake, Chifukwa chake ndinena ndinu, Musade nkhawa ndi moyo wanu, chimene mudzadya; kapena ndi thupi lanu, chimene mudzavala.


Ndipo anati wina, Ine ndakwatira mkazi, ndipo chifukwa chake sindingathe kudza.


chifukwa ali wolipidwa, ndipo sasamala nkhosa.


Mwamunayo apereke kwa mkazi mangawa ake; koma modzimodzinso mkazi kwa mwamuna.


Koma ndifuna kuti mukhale osalabadira. Iye amene wosakwatira alabadira zinthu za Ambuye, kuti akondweretse Ambuye;


Ndi mkazi wokwatiwa ndi namwali asiyananso. Iye wosakwatiwa alabadira za Ambuye, kuti akhale woyera m'thupi ndi mumzimu; koma wokwatiwayo, alabadira za dziko lapansi, kuti akondweretse mwamunayo.


Amuna inu, kondani akazi anu, ndipo musawawire mtima iwo.


Koma ngati wina sadzisungiratu mbumba yake ya iye yekha, makamaka iwo a m'banja lake, wakana chikhulupiriro iye, ndipo aipa koposa wosakhulupirira.


Momwemonso amuna inu, khalani nao monga mwa chidziwitso, ndi kuchitira mkazi ulemu, monga chotengera chochepa mphamvu, monganso wolowa nyumba pamodzi wa chisomo cha moyo, kuti mapemphero anu angaletsedwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa