1 Akorinto 7:29 - Buku Lopatulika29 Koma ichi nditi, abale, yafupika nthawi, kuti tsopano iwo akukhala nao akazi akhalebe monga ngati alibe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Koma ichi nditi, abale, yafupika nthawi, kuti tsopano iwo akukhala nao akazi akhalebe monga ngati alibe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Chimene ndikukuuzani, abale, nchakuti nthaŵi yachepa. Kuyambira tsopano anthu okwatira akhale monga ngati sadakwatire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Abale, chimene ndikutanthauza nʼchakuti nthawi yatha. Kuyambira tsopano anthu okwatira akhale ngati sanakwatire. Onani mutuwo |