Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 6:17 - Buku Lopatulika

17 Koma iye wophatikidwa ndi Ambuye ali mzimu umodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Koma iye wophatikidwa ndi Ambuye ali mzimu umodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Koma amene amadzipereka kwa Ambuye, iyeyo ndi Ambuye amakhala mzimu umodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Koma amene amadzipereka kwa Ambuye, iyeyo ndi Ambuye amakhala mzimu umodzi.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 6:17
9 Mawu Ofanana  

Chobadwa m'thupi chikhala thupi, ndipo chobadwa mwa Mzimu, chikhala mzimu.


Koma inu simuli m'thupi ai, koma mumzimu, ngatitu Mzimu wa Mulungu akhalabe mwa inu. Koma ngati munthu alibe Mzimu wa Khristu, siali wake wa Khristu.


Pakutinso mwa Mzimu mmodzi ife tonse tinabatizidwa kulowa m'thupi limodzi, ngakhale Ayuda, ngakhale Agriki, ngakhale akapolo, ngakhale mfulu; ndipo tonse tinamwetsedwa Mzimu mmodzi.


Kodi simudziwa kuti matupi anu ali ziwalo za Khristu? Chifukwa chake ndidzatenga ziwalo za Khristu kodi, ndi kuziyesa ziwalo za mkazi wachiwerewere? Msatero iai.


Ndinapachikidwa ndi Khristu; koma ndili ndi moyo; wosatinso ine ai, koma Khristu ali ndi moyo mwa ine; koma moyo umene ndili nao tsopano m'thupi, ndili nao m'chikhulupiriro cha Mwana wa Mulungu, amene anandikonda, nadzipereka yekha chifukwa cha ine.


pakuti tili ziwalo za thupi lake.


Mukhale nao mtima m'kati mwanu umene unalinso mwa Khristu Yesu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa