Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 16:24 - Buku Lopatulika

24 Chikondi changa chikhale ndi inu nonse mwa Khristu Yesu. Amen.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Chikondi changa chikhale ndi inu nonse mwa Khristu Yesu. Amen.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Chikondi changa chikhale pa inu nonse, mwa Khristu Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Chikondi changa chikhale ndi nonsenu mwa Khristu Yesu.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 16:24
11 Mawu Ofanana  

ndi kuwaphunzitsa, asunge zinthu zonse zimene ndinakulamulani inu; ndipo onani, Ine ndili pamodzi ndi inu masiku onse, kufikira chimaliziro cha nthawi ya pansi pano.


Ndipo musatitengere kokatiyesa, koma mutipulumutse kwa woipayo.


Chifukwa ngati udalitsa ndi mzimu, nanga iye wakukhala wosaphunzira adzati Amen bwanji, pa kuyamika kwako, popeza sadziwa chimene unena?


Zanu zonse zichitike m'chikondi.


Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu chikhale ndi inu.


Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu, mwa chifuniro cha Mulungu, ndi Timoteo mbaleyo, kwa Mpingo wa Mulungu umene uli ku Korinto, pamodzi ndi oyera mtima onse amene ali mu Akaya monse:


Chifukwa ninji? Chifukwa sindikonda inu kodi? Adziwa Mulungu.


Ndipo ndidzapereka ndi kuperekedwa konse chifukwa cha miyoyo yanu mokondweratu. Ngati ndikonda inu kochuluka koposa, kodi ndikondedwa kochepa?


Pakuti Mulungu ali mboni yanga, kuti ndilakalaka inu nonse m'phamphu la mwa Khristu Yesu.


Onse amene ndiwakonda, ndiwadzudzula ndi kuwalanga; potero chita changu, nutembenuke mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa