1 Akorinto 16:18 - Buku Lopatulika18 Pakuti anatsitsimutsa mzimu wanga ndi wanu; chifukwa chake muzindikire otere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pakuti anatsitsimutsa mzimu wanga ndi wanu; chifukwa chake muzindikire otere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Adandisangulutsa ine monga adasangulutsanso inu. Anthu otere muziŵalemekeza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pakuti anatsitsimutsa mzimu wanga ndi wanu womwe. Anthu a mtundu oterewa ngofunika kuwalemekeza. Onani mutuwo |