1 Akorinto 16:13 - Buku Lopatulika13 Dikirani, chilimikani m'chikhulupiriro, dzikhalitseni amuna, limbikani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Dikirani, chilimikani m'chikhulupiriro, dzikhalitseni amuna, limbikani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Khalani maso, khalani okhazikika m'chikhulupiriro chanu, chitani chamuna, khalani amphamvu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Khalani tcheru; khazikikani mʼchikhulupiriro chanu; limbani mtima; khalani amphamvu. Onani mutuwo |