1 Akorinto 16:11 - Buku Lopatulika11 chifukwa chake munthu asampeputse. Koma mumperekeze mumtendere, kuti akadze kwa ine; pakuti ndimuyembekezera pamodzi ndi abale. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 chifukwa chake munthu asampeputse. Koma mumperekeze mumtendere, kuti akadze kwa ine; pakuti ndimuyembekezera pamodzi ndi abale. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono wina aliyense asamnyoze, koma mumthandize kupitiriza ulendo wake mwamtendere kubwerera kuli ine kuno. Paja ndikumuyembekeza pamodzi ndi abale ena. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Wina aliyense asamunyoze. Muthandizeni kupitiriza ulendo wake mwamtendere kubwereranso kuli ine. Ndikumuyembekeza pamodzi ndi abale ena. Onani mutuwo |