1 Akorinto 15:49 - Buku Lopatulika49 Ndipo monga tavala fanizo la wanthakayo, tidzavalanso fanizo la wakumwambayo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 Ndipo monga tavala fanizo la wanthakayo, tidzavalanso fanizo la wakumwambayo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 Monga takhala ofanafana ndi Adamu, munthu wopangidwa ndi dothi uja, momwemonso tidzakhala ofanafana ndi Khristu, munthu wa Kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 Ndipo monga momwe tinabadwa ofanana ndi munthu wa dziko lapansi uja, momwemonso tidzakhala ofanana ndi munthu wakumwamba. Onani mutuwo |