Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 15:48 - Buku Lopatulika

48 Monga wanthakayo, ateronso anthaka; ndi monga wakumwamba, ateronso akumwamba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

48 Monga wanthakayo, ateronso anthaka; ndi monga wakumwamba, ateronso akumwamba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

48 Anthu onse apansipano ali ngati Adamu wopangidwa ndi dothi uja. Ndipo onse amene ali a Kumwamba, ali ngati Khristu wa Kumwamba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

48 Monga analili munthu wa dziko lapansi, momwemonso anthu onse amene ndi a dziko lapansi. Ndipo monga alili munthu wakumwamba, momwemonso anthu onse amene ndi akumwamba.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 15:48
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Adamu anakhala ndi moyo zaka zana limodzi kudza makumi atatu, nabala mwana wamwamuna m'chifanizo chake; namutcha dzina lake Seti.


Adzatulutsa choyera m'chinthu chodetsa ndani? Nnena mmodzi yense.


Chifukwa chake inu mukhale angwiro, monga Atate wanu wa Kumwamba ali wangwiro.


Chobadwa m'thupi chikhala thupi, ndipo chobadwa mwa Mzimu, chikhala mzimu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa