1 Akorinto 15:47 - Buku Lopatulika47 Munthu woyambayo ali wapansi, wanthaka. Munthu wachiwiri ali wakumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Munthu woyambayo ali wapansi, wanthaka. Munthu wachiwiri ali wakumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Adamu woyamba uja anali wochokera ku dothi, anali wapansipano. Koma Khristu, Adamu wachiŵiri uja, anali wochokera Kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Munthu woyamba anali wa dziko lapansi, wochokera mʼnthaka koma munthu wachiwiri anali wochokera kumwamba. Onani mutuwo |