Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 15:36 - Buku Lopatulika

36 Wopusa iwe, chimene uchifesa wekha sichikhalitsidwanso chamoyo, ngati sichifa;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Wopusa iwe, chimene uchifesa wekha sichikhalitsidwanso chamoyo, ngati sichifa;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Ati kupusa ati! Mbeu imene umafesa, siingamere ndi kukhala moyo itapanda kufa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Wopusa iwe! Chimene mudzala sichikhala ndi moyo pokhapokha chitayamba chafa.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 15:36
9 Mawu Ofanana  

Ngakhale muzu wake wakalamba m'nthaka, ndi tsinde lake likufa pansi.


Opusa inu, kodi Iye wopanga kunja kwake sanapangenso m'kati mwake?


Koma Mulungu anati kwa iye, Wopusa iwe, usiku womwe uno udzafunidwa moyo wako; ndipo zinthu zimene unazikonza zidzakhala za yani?


Ndipo Iye anati kwa iwo, Opusa inu, ndi ozengereza mtima kusakhulupirira zonse adazilankhula aneneri!


Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Ngati mbeu ya tirigu siigwa m'nthaka, nifa, ikhala pa yokha iyo; koma ngati ifa, ibala chipatso chambiri.


Pakunena kuti ali anzeru, anapusa;


ndipo chimene ufesa, sufesa thupi limene lidzakhala, koma mbeu yokha kapena ya tirigu kapena ya mtundu wina;


Potero, penyani bwino umo muyendera, si monga opanda nzeru, koma monga anzeru;


Koma ufuna kuzindikira kodi, munthu wopanda pake iwe, kuti chikhulupiriro chopanda ntchito chili chabe?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa