1 Akorinto 15:34 - Buku Lopatulika34 Ukani molungama, ndipo musachimwe; pakuti ena alibe chidziwitso cha Mulungu. Ndilankhula kunyaza inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ukani molungama, ndipo musachimwe; pakuti ena alibe chidziwitso cha Mulungu. Ndilankhula kunyaza inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Mudzidzimuke mumtima mwanu, ndipo muleke kuchimwa. Ena mwa inu sadziŵa Mulungu konse. Ndikukuuzani zimenezi kuti muchite manyazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Ganizani bwino monga kuyenerera, ndiye lekani kuchimwa; pakuti pali ena amene sadziwa Mulungu. Ndikunena izi kuti muchite manyazi. Onani mutuwo |