Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 15:30 - Buku Lopatulika

30 Nanga ifenso tili m'moopsa bwanji nthawi zonse?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Nanga ifenso tili m'moopsa bwanji nthawi zonse?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Nanga pamenepo ifenso timakhaliranji m'zoopsa nthaŵi zonse?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Ndipo kwa ife, tikuyikiranji moyo wathu pachiswe nthawi ndi nthawi?

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 15:30
8 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mene iwo anali kupita pamadzi, Iye anagona tulo. Ndipo panyanja panatsikira namondwe wa mphepo; ndipo podzala ndi madzi, analimkuopsedwa.


Ngati si kutero, adzachita chiyani iwo amene abatizidwa chifukwa cha akufa? Ngati akufa saukitsidwa konse, abatizidwa chifukwa ninji chifukwa cha iwo?


Ndifa tsiku ndi tsiku, ndilumbira pa kudzitamandira kwa inu, abale, kumene ndili nako mwa Khristu Yesu, Ambuye wathu.


monga osadziwika, angakhale adziwika bwino; monga alinkufa, ndipo taonani tili ndi moyo; monga olangika, ndipo osaphedwa;


Koma ine, abale, ngati ndilalikiranso mdulidwe, ndizunzikanso bwanji? Pamenepo chikhumudwitso cha mtanda chidatha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa